2 Mafumu 7:3 - Buku Lopatulika3 Koma polowera pa chipata panali amuna anai akhate, nanenana wina ndi mnzake, Tikhaliranji kuno mpaka kufa? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Koma polowera pa chipata panali amuna anai akhate, nanenana wina ndi mnzake, Tikhaliranji kuno mpaka kufa? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Nthaŵi imeneyo panali anthu akhate anai amene ankakhala pa chipata. Iwowo adayamba kufunsana kuti, “Chifukwa chiyani tikungotambalala pano kumangodikira imfa? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Tsono pa chipata cholowera mu mzinda wa Samariya pankakhala anthu anayi akhate. Iwo anayankhulana kuti, “Chifukwa chiyani tikungokhala pano kudikira kufa? Onani mutuwo |