2 Mafumu 6:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo wina anati, Mulole mupite nafe anyamata anu. Nati, Ndidzamuka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo wina anati, Mulole mupite nafe anyamata anu. Nati, Ndidzamuka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Apo mmodzi mwa iwo adati, “Bwanji inuyo mupite nafe, atumiki anufe.” Elisa adavomera nati, “Tiyeni.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Mmodzi wa iwo anati, “Chonde mulole kutsagana nawo atumiki anu.” Elisa anayankha kuti, “Ndipita nanu.” Onani mutuwo |