Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Mafumu 6:3 - Buku Lopatulika

3 Ndipo wina anati, Mulole mupite nafe anyamata anu. Nati, Ndidzamuka.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Ndipo wina anati, Mulole mupite nafe anyamata anu. Nati, Ndidzamuka.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Apo mmodzi mwa iwo adati, “Bwanji inuyo mupite nafe, atumiki anufe.” Elisa adavomera nati, “Tiyeni.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Mmodzi wa iwo anati, “Chonde mulole kutsagana nawo atumiki anu.” Elisa anayankha kuti, “Ndipita nanu.”

Onani mutuwo Koperani




2 Mafumu 6:3
8 Mawu Ofanana  

Koma make wa mwana anati, Pali Yehova, pali inunso, ngati nkukusiyani. Ndipo ananyamuka, namtsata.


Nati Naamani, Ulole ulandire matalente awiri. Namkakamiza namanga matalente awiri a siliva m'matumba awiri, ndi zovala zosintha ziwiri, nasenzetsa anyamata ake awiri; iwo anatsogola atazisenza.


Mutilole tipite ku Yordani, tikatengeko aliyense mtengo, tidzimangire malo komweko, tikhalepo. Nati, Mukani.


Namuka nao, nafika ku Yordani, iwo natema mitengo.


Koma tsopano balindani, mundipenyerere; ndikanena bodza pamaso panu mudzalizindikira.


Ndipo ananena ndi Iye, Ikapanda kumuka nane nkhope yanu, musatikweze kuchokera kuno.


Nakhala pansi nadya namwa onse awiri pamodzi; nati kwa munthuyo atate wa mkaziyo, Uvomere, ugone kuno usiku, nusekerere mtima wako.


Ndipo Baraki anati kwa iye, Ukamuka nane, ndidzamuka; ukapanda kumuka nane, sindimuka.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa