Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mafumu 6:2 - Buku Lopatulika

2 Mutilole tipite ku Yordani, tikatengeko aliyense mtengo, tidzimangire malo komweko, tikhalepo. Nati, Mukani.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Mutilole tipite ku Yordani, tikatengeko aliyense mtengo, tidzimangire malo komweko, tikhalepo. Nati, Mukani.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Mutilole tipite ku Yordani, tikadule nsichi imodzi-imodzi, kuti tidzakonze malo oti tizikhalamo.” Elisa adayankha kuti, “Chabwino, pitani.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Tiloleni tipite ku Yorodani kumene aliyense wa ife akadule mtengo umodzi, kuti timange malo woti tizikhalamo.” Ndipo Elisa anati, “Pitani.”

Onani mutuwo Koperani




2 Mafumu 6:2
9 Mawu Ofanana  

Ndipo ana a aneneri anati kwa Elisa, Taonani tsono, pamalo tikhalapo ife pamaso panu patichepera


Ndipo wina anati, Mulole mupite nafe anyamata anu. Nati, Ndidzamuka.


Simoni Petro ananena nao, Ndinka kukasodza. Ananena naye, Ifenso tipita nawe. Anatuluka, nalowa m'ngalawa; ndipo mu usiku muja sanagwire kanthu.


ndipo popeza anali wa ntchito imodzimodzi, anakhala nao, ndipo iwowa anagwira ntchito; pakuti ntchito yao inali yakusoka mahema.


Kapena kodi ife tokha, Barnabasi ndi ine tilibe ulamuliro wakusagwira ntchito?


Pakuti mukumbukira, abale, chigwiritso chathu ndi chivuto chathu; pochita usiku ndi usana, kuti tingalemetse wina wa inu, tinalalikira kwa inu Uthenga Wabwino wa Mulungu.


kapena sitinadye mkate chabe padzanja la munthu aliyense, komatu m'chivuto ndi chipsinjo, tinagwira ntchito usiku ndi usana, kuti tingalemetse wina wa inu;


Koma chipembedzo pamodzi ndi kudekha chipindulitsa kwakukulu;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa