2 Mafumu 6:4 - Buku Lopatulika4 Namuka nao, nafika ku Yordani, iwo natema mitengo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Namuka nao, nafika ku Yordani, iwo natema mitengo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Choncho Elisayo adapita nawo. Atafika ku Yordani, anthu aja adayamba kudula mitengo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Ndipo anapita nawo. Anapita ku Yorodani nayamba kudula mitengo. Onani mutuwo |