2 Mafumu 5:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo analowa wina, nauza mbuye wake, kuti, Buthulo lofuma ku dziko la Israele lanena zakutizakuti. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo analowa wina, nauza mbuye wake, kuti, Buthulo lofuma ku dziko la Israele lanena zakutizakuti. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Naamani atamva zimene adaanena mtsikana uja, adapita kwa mfumu nakaiuza kuti, “Mtsikana amene tidakagwira ku Israele uja wanena kuti ati ndipite ku Samariya, kuti mneneri wakumeneko akandichize.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Naamani anapita kwa mbuye wake kukamuwuza zomwe mtsikana wochokera ku Israeli ananena. Onani mutuwo |