2 Mafumu 5:3 - Buku Lopatulika3 Nati uyu kwa mbuyake wamkazi, Mbuye wanga akadakhala kwa mneneri ali mu Samariya, akadamchiritsa khate lake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Nati uyu kwa mbuyake wamkazi, Mbuye wanga akadakhala kwa mneneri ali m'Samariya, akadamchiritsa khate lake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Tsono mtsikana uja adauza mkazi wa Naamani kuti, “Bwanji kodi osati ambuyanga apite kwa mneneri ku Samariya, kuti mneneriyo akaŵachize khate laoli.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Mtsikanayo anawuza mkazi wa Naamani kuti, “Mbuye wanga akanapita kukaonana ndi mneneri amene amakhala ku Samariya, akanachiritsidwa khate lawo.” Onani mutuwo |