2 Mafumu 5:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo Aaramu adatuluka magulumagulu, nabwera nalo m'ndende buthu lochokera ku dziko la Israele, natumikira mkazi wa Naamani iyeyu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo Aaramu adatuluka magulumagulu, nabwera nalo m'ndende buthu lochokera ku dziko la Israele, natumikira mkazi wa Naamani iyeyu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Nthaŵi ina Asiriya adaagwirako mtsikana ku dziko la Israele kumene adakathirako nkhondo, ndipo mtsikanayo adasanduka mdzakazi wa mkazi wa Naamani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Tsono magulu a Aaramu anapita ku nkhondo ndipo anakagwira ukapolo mtsikana wamngʼono wa ku Israeli, ndipo ankatumikira mkazi wa Naamani. Onani mutuwo |