Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Mafumu 4:5 - Buku Lopatulika

5 Pamenepo anamchokera, nadzitsekera yekha ndi ana ake aamuna; iwo namtengera zotengerazo, iye namatsanulira.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Pamenepo anamchokera, nadzitsekera yekha ndi ana ake amuna; iwo namtengera zotengerazo, iye namatsanulira.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Mai uja adachoka kwa Elisayo, nakadzitsekera ndi ana ake aŵiri aja. Tsono iyeyo ankati akathira mafuta m'mbiya nidzaza, ana ake ankabwera ndi mbiya ina.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Mayi uja anachoka kwa Elisa nakadzitsekera ndi ana ake. Anthu anabweretsa mitsuko kwa iye ndipo ankathiramo mafuta.

Onani mutuwo Koperani




2 Mafumu 4:5
6 Mawu Ofanana  

Nulowe, nudzitsekere wekha ndi ana ako aamuna ndi kutsanulira m'zotengera zonsezi, nuike padera zodzalazo.


Ndipo kunali, zitadzala zotengera, anati kwa mwana wake, Nditengere chotengera china. Nanena naye, Palibe chotengera china. Ndipo mafuta analeka.


Koma Naamani adapsa mtima, nachoka, nati, Taona, ndinati m'mtima mwanga, kutuluka adzanditulukira, nadzaima ndi kuitana pa dzina la Yehova Mulungu wake, ndi kuweyula dzanja lake pamalopo, ndi kuchiritsa wakhateyo.


Ndipo wodala ali iye amene anakhulupirira; chifukwa zidzachitidwa zinthu zimene Ambuye analankhula naye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa