2 Mafumu 3:3 - Buku Lopatulika3 Koma anakangamira zoipa za Yerobowamu mwana wa Nebati, zimene anachimwitsa nazo Israele, osalekana nazo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Koma anakangamira zoipa za Yerobowamu mwana wa Nebati, zimene anachimwitsa nazo Israele, osalekana nazo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Komabe adaumirira kuchita zoipa zomwe ankachita Yerobowamu, mwana wa Nebati, zimene adaachimwitsa nazo Aisraele, osafuna konse kuzileka. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Komabe anawumirira kuchita machimo a Yeroboamu mwana wa Nebati, amene anachimwitsa nawo Israeli ndipo sanafune kuwaleka. Onani mutuwo |