2 Mafumu 17:3 - Buku Lopatulika3 Anamkwerera Salimanezere mfumu ya Asiriya kumthira nkhondo; ndipo Hoseya anamgonjera, namsonkhera mitulo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Anamkwerera Salimanezere mfumu ya Asiriya kumthira nkhondo; ndipo Hoseya anamgonjera, namsonkhera mitulo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Salimanezere, mfumu ya ku Asiriya, adadza kudzamthira nkhondo, ndipo Hoseya adamgonjera, namakhoma msonkho kwa iyeyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Salimenezeri mfumu ya ku Asiriya anabwera kudzathira nkhondo Hoseya amene anali pansi pa ulamuliro wake ndipo ankapereka msonkho kwa iyeyo. Onani mutuwo |
Ndipo tsono, Mulungu wathu, ndinu Mulungu wamkulu, ndi wamphamvu, ndi woopsa, wakusunga pangano ndi chifundo, asachepe pamaso panu mavuto athu onse amene anatigwera ife, ndi mafumu athu, akulu athu, ndi ansembe athu, ndi aneneri athu, ndi makolo athu, ndi anthu anu onse, kuyambira masiku a mafumu a Asiriya, mpaka lero lino.