2 Mafumu 17:2 - Buku Lopatulika2 Nachita iye choipa pamaso pa Yehova, koma osati monga mafumu a Israele asanakhale iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Nachita iye choipa pamaso pa Yehova, koma osati monga mafumu a Israele asanakhale iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Tsono adachita zoipa kuchimwira Chauta, komabe osalingana ndi mafumu a ku Israele amene ankalamulira, iyeyo asanaloŵe ufumu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Iye anachita zoyipa pamaso pa Yehova, koma osafanana ndi mafumu a Israeli amene ankalamulira iye asanalowe ufumuwo. Onani mutuwo |