2 Mafumu 17:1 - Buku Lopatulika1 Chaka chakhumi ndi ziwiri cha Ahazi mfumu ya Yuda Hoseya mwana wa Ela analowa ufumu wake wa Israele mu Samariya, nakhala mfumu zaka zisanu ndi zinai. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Chaka chakhumi ndi ziwiri cha Ahazi mfumu ya Yuda Hoseya mwana wa Ela analowa ufumu wake wa Israele m'Samariya, nakhala mfumu zaka zisanu ndi zinai. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Chaka cha 12 cha ufumu wa Ahazi mfumu ya ku Yuda, Hoseya mwana wa Ela adaloŵa ufumu wa ku Israele ku Samariya. Ndipo adalamulira zaka zisanu ndi zinai. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Mʼchaka cha 12 cha Ahazi mfumu ya Yuda, Hoseya mwana wa Ela anakhala mfumu ya Israeli mu Samariya ndipo analamulira zaka zisanu ndi zinayi. Onani mutuwo |