2 Mafumu 12:3 - Buku Lopatulika3 Koma misanje sanaichotse; anthu anapherabe nsembe, nafukiza kumisanje. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Koma misanje sanaichotse; anthu anapherabe nsembe, nafukiza kumisanje. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Komabe akachisi opembedzerako mafano pa zitunda sadaŵaononge. Anthu adapitirirabe kupereka nsembe ndi kumafukiza lubani pa malo amenewo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Komabe sanachotse malo opembedzerapo mafano ndipo anthu anapitiriza kupereka nsembe ndi kufukiza lubani ku malo opembedzerako mafanowo. Onani mutuwo |