2 Mafumu 12:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo Yowasi anachita zoongoka pamaso pa Yehova masiku ake onse, m'mene anamlangizira wansembe Yehoyada. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo Yowasi anachita zoongoka pamaso pa Yehova masiku ake onse, m'mene anamlangizira wansembe Yehoyada. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Tsono Yowasiyo adachita zolungama pamaso pa Chauta masiku onse a moyo wake, chifukwa choti Yehoyada, wansembe uja, ankamlangiza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Yowasi anachita zolungama pamaso pa Yehova masiku onse amene wansembe Yehoyada ankamulangiza. Onani mutuwo |