Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Mafumu 1:5 - Buku Lopatulika

5 Ndipo mithenga inabwerera kwa iye, nanena nayo, Mwabwerera chifukwa ninji?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Ndipo mithenga inabwerera kwa iye, nanena nayo, Mwabwerera chifukwa ninji?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Amithenga aja adabwerera kwa mfumu. Tsono mfumuyo idaŵafunsa kuti, “Chifukwa chiyani mwabwerera?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Amithenga aja atabwerera kwa mfumu, mfumuyo inawafunsa kuti, “Chifukwa chiyani mwabwerera?”

Onani mutuwo Koperani




2 Mafumu 1:5
2 Mawu Ofanana  

Chifukwa chake atero Yehova, Sudzatsika pakama pamene wakwerapo, koma udzafa ndithu. Nachoka Eliya.


Ndipo inanena naye, Munthu anakwera kukomana nafe, nati kwa ife, Kabwerereni kwa mfumu imene inakutumani inu, nimunene nayo, Atero Yehova, Kodi ndi popeza palibe Mulungu mwa Israele, kuti ulikutuma kukafunsira kwa Baala-Zebubi mulungu wa ku Ekeroni? Chifukwa chake sudzatsika pakama pamene wakwerapo, koma udzafa ndithu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa