2 Akorinto 8:20 - Buku Lopatulika20 ndi kupewa ichi kuti wina angatitchule za kuchulukira kumene tikutumikira; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 ndi kupewa ichi kuti wina angatitchule za kuchulukira kumene tikutumikira; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Sitikufuna kupatsa anthu chifukwa choti azitinenera zoipa pa mayendetsedwe athu a zopereka zachifundo zochulukazi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Tikufuna kupewa kutikayikira kulikonse za mmene tikuyendetsera mphatso zochulukazi. Onani mutuwo |