2 Akorinto 8:17 - Buku Lopatulika17 Pakutitu analandira kudandaulira kwathu; koma pokhala nalo khama loposa, anatulukira kunka kwa inu mwini wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Pakutitu analandira kudandaulira kwathu; koma pokhala nalo khama loposa, anatulukira kunka kwa inu mwini wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Pakuti sadangochita zimene tidampempha, koma changu chake chinali chachikulu, kotero kuti adatsimikiza yekha zobwera kwanuko. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Pakuti Tito sanangovomera kokha pempho lathu, koma yekha anafunitsitsa kwambiri kubwera kwa inu mwa iye yekha. Onani mutuwo |