2 Akorinto 8:16 - Buku Lopatulika16 Koma ayamikike Mulungu, wakupatsa khama lomweli la kwa inu mu mtima wa Tito. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Koma ayamikike Mulungu, wakupatsa khama lomweli la kwa inu mu mtima wa Tito. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Tiyamike Mulungu kuti adaika mumtima mwa Tito changu chomwecho chimene ife tili nacho pokuthandizani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Tithokoze Mulungu amene anayika mu mtima wa Tito changu chomwecho chimene ine ndili nacho pa inu. Onani mutuwo |