2 Akorinto 7:7 - Buku Lopatulika7 koma si ndi kufika kwake kokha, komanso ndi chitonthozo chimene anatonthozedwa nacho mwa inu, pamene anatiuza ife kukhumbitsa kwanu, kulira kwanu, changu chanu cha kwa ine; kotero kuti ndinakondwera koposa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 koma si ndi kufika kwake kokha, komanso ndi chitonthozo chimene anatonthozedwa nacho mwa inu, pamene anatiuza ife kukhumbitsa kwanu, kulira kwanu, changu chanu cha kwa ine; kotero kuti ndinakondwera koposa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Ndipo chimene chidatilimbitsa, si kufika kwake kokha, koma makamakanso mau ake onena za m'mene iyeyo mudamlimbitsira mtima. Adatiwuza kuti mukulakalaka kundiwona, kuti muli ndi chisoni, ndiponso kuti mukuchita changu kundithandiza. Nchifukwa chake ndakondwa koposa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 sikubwera kwake kokhako, komanso mawu achilimbikitso amene analandira kuchokera kwa inu. Iye anatiwuza kuti mukufuna kundiona, zachisoni chanu chachikulu, ndi kudzipereka kwanu kwa ine, motero chimwemwe changa chinachuluka kuposa kale. Onani mutuwo |