2 Akorinto 6:6 - Buku Lopatulika6 m'mayeredwe, m'chidziwitso, m'chilekerero, m'kukoma mtima, mwa Mzimu Woyera, m'chikondi chosanyenga; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 m'mayeredwe, m'chidziwitso, m'chilekerero, m'kukoma mtima, mwa Mzimu Woyera, m'chikondi chosanyenga; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Timatsimikiza kuti ndife atumiki a Mulungu pakuyera mtima, pakudziŵa zinthu mozama, pakuleza mtima, pakukoma mtima, mwa Mzimu Woyera, mwa chikondi chosanyenga, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 pokhala moyo woyera mtima, pomvetsa zinthu, wokoma mtima ndi wachifundo mwa Mzimu Woyera ndi mwachikondi choonadi Onani mutuwo |