2 Akorinto 6:5 - Buku Lopatulika5 m'mikwingwirima, m'ndende, m'maphokoso, m'mavutitso, m'madikiro, m'masalo a chakudya; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 m'mikwingwirima, m'ndende, m'maphokoso, m'mavutitso, m'madikiro, m'masalo a chakudya; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Tidakwapulidwa, tidaponyedwa m'ndende, ndipo anthu adatiwukira mwachipolowe. Tidagwira ntchito kwambiri, mwina osagona tulo, osaona chakudya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Pomenyedwa, kuponyedwa mʼndende ndi mʼzipolowe. Pogwira ntchito mwamphamvu, posagona usiku onse, posowa chakudya; Onani mutuwo |