2 Akorinto 6:7 - Buku Lopatulika7 m'mau a choonadi, mu mphamvu ya Mulungu; mwa zida za chilungamo kulamanja ndi kulamanzere, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 m'mau a choonadi, mu mphamvu ya Mulungu; mwa zida za chilungamo kulamanja ndi kulamanzere, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 mwa mau oona, ndiponso mwa mphamvu ya Mulungu. Zida zimene zili m'dzanja lathu lamanja ndi lamanzere ndizo chilungamo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 ndi poyankhula choonadi mwamphamvu ya Mulungu. Zida zimene zili mʼdzanja lamanja ndi lamanzere ndizo chilungamo. Onani mutuwo |