2 Akorinto 6:12 - Buku Lopatulika12 Simupsinjika mwa ife, koma mupsinjika mumtima mwanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Simupsinjika mwa ife, koma mupsinjika mumtima mwanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Malo sakusoŵani mumtima mwathu, koma mumtima mwanu ndimo mukusoŵa malo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Ife sitikukubisirani chikondi chathu pa inu, koma inu mukubisa chikondi chanu pa ife. Onani mutuwo |