Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Akorinto 6:12 - Buku Lopatulika

12 Simupsinjika mwa ife, koma mupsinjika mumtima mwanu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Simupsinjika mwa ife, koma mupsinjika mumtima mwanu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Malo sakusoŵani mumtima mwathu, koma mumtima mwanu ndimo mukusoŵa malo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Ife sitikukubisirani chikondi chathu pa inu, koma inu mukubisa chikondi chanu pa ife.

Onani mutuwo Koperani




2 Akorinto 6:12
9 Mawu Ofanana  

Inde akadakukopani muchoke posaukira, mulowe kuchitando kopanda chopsinja; ndipo zoikidwa pagome panu zikadakhala zonona ndithu.


Mapazi ako sadzaombana ulikuyenda; ukathamanga, sudzaphunthwa.


Kupenya kwa maso kuposa kukhumba kwa mtima; ichinso ndi chabe ndi kungosautsa mtima.


Kodi adzati, Nyumba ya Yakobo iwe, Mzimu wa Yehova waperewera kodi? Izi ndi ntchito zake kodi? Mau anga samchitira zokoma kodi, iye amene ayenda choongoka?


Pakuti chipata chili chopapatiza, ndi ichepetsa njirayo yakumuka nayo kumoyo, ndimo akuchipeza chimenecho ali owerengeka.


ndife osautsika monsemo, koma osapsinjika; osinkhasinkha, koma osakhala kakasi;


Tipatseni malo; sitinamchitire munthu chosalungama, sitinaipse munthu, sitinachenjerere munthu.


Pakuti Mulungu ali mboni yanga, kuti ndilakalaka inu nonse m'phamphu la mwa Khristu Yesu.


Koma iye amene ali nacho chuma cha dziko lapansi, naona mbale wake ali wosowa ndi kutsekereza chifundo chake pommana iye, nanga chikondi cha Mulungu chikhala mwa iye bwanji?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa