2 Akorinto 6:13 - Buku Lopatulika13 Ndipo kukhale chibwezero chomwechi (ndinena monga ndi ana anga) mukulitsidwe inunso. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndipo kukhale chibwezero chomwechi (ndinena monga ndi ana anga) mukulitsidwe inunso. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Ndikulankhula nanu ngati ana anga. Mutibwezere zomwezo zimene ifenso tidakuchitirani inu, pakutitsekulira mtima wanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Pofuna kufanana zochita ndi kuyankhula monga kwa ana anga, nanunso muzinena za kukhosi kwanu. Onani mutuwo |