2 Akorinto 6:11 - Buku Lopatulika11 M'kamwa mwathu mmotseguka kwa inu Akorinto, mtima wathu wakulitsidwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 M'kamwa mwathu mmotseguka kwa inu Akorinto, mtima wathu wakulitsidwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Inu anthu a ku Korinto, talankhula nanu momasuka, ndipo tatsekula mtima wathu ndithu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Tayankhula momasuka kwa inu, Akorinto, ndipo tanena zonse za kumtima kwathu. Onani mutuwo |