2 Akorinto 6:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo ochita naye pamodzi tidandauliranso kuti musalandire chisomo cha Mulungu kwachabe inu, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo ochita naye pamodzi tidandauliranso kuti musalandire chisomo cha Mulungu kwachabe inu, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Tsono popeza kuti ndife ogwirizana ndi Mulungu pa ntchito yake, takupembani musaŵasandutse achabe madalitso amene Mulungu adakupatsani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Pogwira naye ntchito pamodzi, tikukudandaulirani kuti musangolandira chisomo cha Mulungu pachabe. Onani mutuwo |