2 Akorinto 3:14 - Buku Lopatulika14 koma mitima yao inaumitsidwa; pakuti kufikira lero lomwe lino, pa kuwerenga kwa pangano lakale chophimba chomwechi chikhalabe chosavundukuka, chimene chilikuchotsedwa mwa Khristu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 koma mitima yao inaumitsidwa; pakuti kufikira lero lomwe lino, pa kuwerenga kwa pangano lakale chophimba chomwechi chikhalabe chosavundukuka, chimene chilikuchotsedwa mwa Khristu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Koma iwo nzeru zao zidauma, pakuti mpaka lero lino chophimba chomwe chija chimakhalapobe akamaŵerenga mabuku a m'Chipangano Chakale. Pajatu chophimbacho chimachotsedwa pokhapokha munthu akakhala mwa Khristu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Koma nzeru zawo zinawumitsidwa, pakuti mpaka lero chophimbira chomwecho chikanalipo pamene akuwerenga Chipangano Chakale. Sichinachotsedwebe, chifukwa chimachotsedwa ngati munthuyo ali mwa Khristu yekha. Onani mutuwo |