Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Akorinto 3:11 - Buku Lopatulika

11 Pakuti ngati chimene chilikuchotsedwa chinakhala mu ulemerero, makamaka kwambiri chotsalacho chili mu ulemerero.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Pakuti ngati chimene chilikuchotsedwa chinakhala m'ulemerero, makamaka kwambiri chotsalacho chili m'ulemerero.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 Tsono ngati zinthu zosakhalitsa zidaafika ndi ulemerero, ndiye kuti zinthu zokhala mpaka muyaya zidzakhala ndi ulemerero wopambana.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 Ndipo ngati zosakhalitsa zinabwera ndi ulemerero, koposa kotani ulemerero wamuyayawo!

Onani mutuwo Koperani




2 Akorinto 3:11
8 Mawu Ofanana  

Pakutinso chimene chinachitidwa cha ulemerero sichinachitidwe cha ulemerero m'menemo, chifukwa cha ulemerero woposawo.


Pokhala nacho tsono chiyembekezo chotere, tilankhula ndi kukhazikika mtima kwakukulu,


Chifukwa chake popeza tili nao utumiki umene, monga talandira chifundo, sitifooka;


Pakunena Iye, Latsopano, anagugitsa loyambali. Koma chimene chilinkuguga ndi kusukuluka, chayandikira kukanganuka.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa