Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Akorinto 2:6 - Buku Lopatulika

6 Kwa wotereyo chilango ichi chidachitika ndi ambiri chikwanira;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Kwa wotereyo chilango ichi chidachitika ndi ambiri chikwanira;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Munthu woteroyo, pafupi nonse mwamtsutsa, choncho chilangocho nchokwanira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Chilango chimene ambiri a inu mwamupatsa munthu ameneyu nʼchokwanira.

Onani mutuwo Koperani




2 Akorinto 2:6
4 Mawu Ofanana  

Chifukwa cha ichi ndilembera izi pokhala palibe ine, kuti pokhala ndili pomwepo ndingachite mowawitsa, monga mwa ulamuliro umene Ambuye anandipatsa ine wakumangirira, ndipo si wakugwetsa.


Pakuti, taonani, ichi chomwe, chakuti mudamvetsedwa chisoni cha kwa Mulungu, khama lalikulu lanji chidalichita mwa inu, komanso chodzikonza, komanso mkwiyo, komanso mantha, komanso kukhumbitsa komanso changu, komanso kubwezera chilango! M'zonse munadzitsimikizira nokha kuti muli oyera mtima m'menemo.


Iwo akuchimwa uwadzudzule pamaso pa onse, kuti otsalawo achite mantha.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa