Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Akorinto 12:3 - Buku Lopatulika

3 Ndipo ndidziwa munthu wotereyo (ngati m'thupi, ngati wopanda thupi, sindidziwa; adziwa Mulungu),

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Ndipo ndidziwa munthu wotereyo (ngati m'thupi, ngati wopanda thupi, sindidziwa; adziwa Mulungu),

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Ndikudziŵa kuti munthuyo adaatengedwa mwadzidzidzi kupita ku Paradizo. Sindikudziŵa ngati zimenezi zidaachitika ali m'thupi, kapena ali kunja kwa thupi. Akudziŵa ndi Mulungu zimenezi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Ndipo ndikumudziwa munthu ameneyu. Sindikudziwa ngati zinachitika mʼthupi kapena ayi, zimenezo akudziwa ndi Mulungu.

Onani mutuwo Koperani




2 Akorinto 12:3
3 Mawu Ofanana  

Ndipo Iye ananena naye, Indetu, ndinena ndi iwe, Lero lino udzakhala ndine mu Paradaiso.


Chifukwa ninji? Chifukwa sindikonda inu kodi? Adziwa Mulungu.


Ndidziwa munthu wa mwa Khristu, zitapita zaka khumi ndi zinai (ngati m'thupi, sindidziwa; ngati kunja kwa thupi, sindidziwa; adziwa Mulungu), anakwatulidwa wotereyo kunka naye Kumwamba kwachitatu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa