2 Akorinto 12:17 - Buku Lopatulika17 Kodi wina wa iwo ndinawatuma kwa inu, ndinakuchenjererani naye kodi? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Kodi wina wa iwo ndinawatuma kwa inu, ndinakuchenjererani naye kodi? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Kodi kapena ndidakuchenjererani mwa aliyense amene ndidamtuma kwa inu? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Kodi ndinakudyerani masuku pamutu kudzera mwa wina aliyense amene ndinamutumiza kwa inu? Onani mutuwo |