Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Akorinto 11:5 - Buku Lopatulika

5 Pakuti ndiyesa kuti sindinaperewere konse ndi atumwi oposatu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Pakuti ndiyesa kuti sindinaperewera konse ndi atumwi oposatu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Ndikuganiza kuti atumwi anu apamwambawo sandiposa ine pa kanthu kalikonse.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Komatu sindikuganiza kuti ndine wotsika kwambiri kwa “atumwi apamwamba.”

Onani mutuwo Koperani




2 Akorinto 11:5
3 Mawu Ofanana  

Koma ndi chisomo cha Mulungu ndili ine amene ndili; ndipo chisomo chake cha kwa ine sichinakhale chopanda pake, koma ndinagwirira ntchito yochuluka ya iwo onse; koma si ine, koma chisomo cha Mulungu chakukhala ndi ine.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa