2 Akorinto 11:25 - Buku Lopatulika25 Katatu ndinamenyedwa ndi ndodo, kamodzi ndinaponyedwa miyala, katatu ndinatayika posweka chombo, ndinakhala m'kuya tsiku limodzi usana ndi usiku; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Katatu ndinamenyedwa ndi ndodo, kamodzi ndinaponyedwa miyala, katatu ndinatayika posweka chombo, ndinakhala m'kuya tsiku limodzi usana ndi usiku; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Katatu Aroma adandimenya ndi ndodo. Kamodzi anthu adandiponya miyala. Katatu pa maulendo athu apanyanja, chombo chathu chidasweka. Nthaŵi ina ndidayandama pakati pa nyanja tsiku lathunthu, usana ndi usiku. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Katatu anandimenya ndi ndodo. Kamodzi anandigendapo miyala. Katatu sitima yathu ya panyanja inasweka, ndipo ndinakhala usiku ndi usana ndi kuyandama pa nyanja. Onani mutuwo |