2 Akorinto 11:18 - Buku Lopatulika18 Popeza ambiri adzitamandira monga mwa thupi, inenso ndidzadzitamandira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Popeza ambiri adzitamandira monga mwa thupi, inenso ndidzadzitamandira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Tsono popeza kuti ambiri akunyadira zapansipano, inenso ndidzatero. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Popeza ambiri akudzitama monga dziko lapansi limachitira, inenso ndidzitamanso. Onani mutuwo |