2 Akorinto 11:10 - Buku Lopatulika10 Choonadi cha Khristu chili mwa ine, kuti kudzitamandira kumene sikudzaletsedwa kwa ine mu mbali za Akaya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Choonadi cha Khristu chili mwa ine, kuti kudzitamandira kumene sikudzaletsedwa kwa ine mu mbali za Akaya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Malinga ndi choona cha Khristu chimene chili mwa ine, ndikunenetsa kuti palibe munthu amene adzandiletsa kunyadira zimenezi m'madera onse a ku Akaiya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Kunena moona mtima molingana ndi chilungamo cha Khristu chimene chili mwa ine, palibe amene angandiletse kudzitamandira mʼzigawo za ku Akaya. Onani mutuwo |