2 Akorinto 10:14 - Buku Lopatulika14 Pakuti sitinyanyampiradi tokha, monga ngati sitinafikire kwa inu; pakuti tinadza kufikira inunso, mu Uthenga Wabwino wa Khristu: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Pakuti sitinyanyampiradi tokha, monga ngati sitinafikira kwa inu; pakuti tinadza kufikira inunso, mu Uthenga Wabwino wa Khristu: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Sitidabzole malire athu, monga ngati sitidakafike kwanu. Tinali oyamba ndife kukafika kwanu ndi kulalika Uthenga Wabwino wonena za Khristu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Pakuti sitikudzitama modutsa malire ngati kuti sitinafike kwa inu, popeza tinali oyamba kufika kwa inu ndi Uthenga Wabwino wa Khristu. Onani mutuwo |