2 Akorinto 10:13 - Buku Lopatulika13 Koma ife sitidzadzitamandira popitirira muyeso, koma monga mwa muyeso wa chilekezero chimene Mulungu anatigawira muyeso, kufikira ngakhale kwa inunso. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Koma ife sitidzadzitamandira popitirira muyeso, koma monga mwa muyeso wa chilekezero chimene Mulungu anatigawira muyeso, kufikira ngakhale kwa inunso. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Kunena za ife, sitinganyade mopitirira malire. Tidzasamala malire omwe Mulungu adatiikira potifikitsa mpaka kwa inu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Komabe, ifeyo sitidzitama modutsa malire ake enieni, koma kudzitama kwathu kudzalekeza mʼmalire amene Mulungu anatiyikira, malire ake ndi mpaka kwa inu. Onani mutuwo |