2 Akorinto 1:22 - Buku Lopatulika22 amenenso anatisindikiza chizindikiro, natipatsa chikole cha Mzimu mu mitima yathu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 amenenso anatisindikiza chizindikiro, natipatsa chikole cha Mzimu mu mitima yathu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 natisindikiza chizindikiro chake, ndi kuika Mzimu Woyera m'mitima mwathu ngati chikole. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 nayikanso Mzimu wake mʼmitima mwathu kutitsimikizira za mʼtsogolo. Onani mutuwo |