2 Akorinto 1:23 - Buku Lopatulika23 Koma ine ndiitana Mulungu akhale mboni pa moyo wanga, kuti kulekera inu ndinaleka kudza ku Korinto. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Koma ine ndiitana Mulungu akhale mboni pa moyo wanga, kuti kulekera inu ndinaleka kudza ku Korinto. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Mulungu akhale mboni yanga, chifukwa chenicheni chimene sindidafikirenso ku Korinto chinali chakuti ndisakumvetseni chisoni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Mulungu ndi mboni yanga kuti sindinabwererenso ku Korinto kuno kuti ndisakumvetseni chisoni. Onani mutuwo |