2 Akorinto 1:21 - Buku Lopatulika21 Koma Iye wakutikhazika pamodzi ndi inu kwa Khristu, natidzoza ife, ndiye Mulungu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Koma Iye wakutikhazika pamodzi ndi inu kwa Khristu, natidzoza ife, ndiye Mulungu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Mulungu ndi amene amatikhazikitsa pamodzi nanu mwa Khristu. Ndiye amene adatidzoza, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Tsono ndi Mulungu amene anachititsa kuti inu ndi ife tiyime molimba mwa Khristu. Anatidzoza ife, Onani mutuwo |