1 Yohane 5:9 - Buku Lopatulika9 Ngati tilandira umboni wa anthu, umboni wa Mulungu uposa; chifukwa umboni wa Mulungu ndi uwu, kuti anachita umboni za Mwana wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ngati tilandira umboni wa anthu, umboni wa Mulungu uposa; chifukwa umboni wa Mulungu ndi uwu, kuti anachita umboni za Mwana wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Timalandira umboni wa anthu, koma umboni wa Mulungu ndi wopambana umboni wa anthu. Umboniwo ndi umene Mulungu adachitira Mwana wake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Timalandira umboni wa anthu, koma umboni wa Mulungu ndi wopambana. Umboniwo ndi umene anachitira Mwana wake. Onani mutuwo |