Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Yohane 5:8 - Buku Lopatulika

8 Mzimu, ndi madzi, ndi mwazi; ndipo iwo atatu ali mmodzi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Mzimu, ndi madzi, ndi mwazi; ndipo iwo atatu ali mmodzi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Mzimu Woyera, madzi ndi magazi, ndipo atatuŵa amavomerezana.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Mzimu Woyera, madzi ndi magazi; ndipo atatu amavomerezana.

Onani mutuwo Koperani




1 Yohane 5:8
14 Mawu Ofanana  

Chifukwa chake mukani, phunzitsani anthu a mitundu yonse, ndi kuwabatiza iwo m'dzina la Atate, ndi la Mwana, ndi la Mzimu Woyera:


Pakuti ambiri anamchitira umboni wonama, ndipo umboni wao sunalingane.


Koma pamene wafika Nkhoswe, amene Ine ndidzamtuma kwa inu kuchokera kwa Atate, ndiye Mzimu wa choonadi, amene atuluka kwa Atate, Iyeyu adzandichitira Ine umboni.


koma mmodzi wa asilikali anamgwaza ndi nthungo m'nthiti yake, ndipo panatuluka pomwepo mwazi ndi madzi.


Ndipo mau a aneneri avomereza pamenepo; monga kunalembedwa,


Mzimu yekha achita umboni pamodzi ndi mzimu wathu, kuti tili ana a Mulungu;


amenenso anatisindikiza chizindikiro, natipatsa chikole cha Mzimu mu mitima yathu.


Mwa ichi Yesunso, kuti akayeretse anthuwo mwa mwazi wa Iye yekha, adamva chowawa kunja kwa chipata.


Pakuti sikutheka kuwakonzanso, atembenuke mtima, iwo amene anaunikidwa pa nthawi yake, nalawa mphatso ya Kumwamba, nakhala olandirana naye Mzimu Woyera,


chimenenso chifaniziro chake chikupulumutsani tsopano, ndicho ubatizo, kosati kutaya kwa litsiro lake la thupi, komatu funso lake la chikumbumtima chokoma kwa Mulungu, mwa kuuka kwa Yesu Khristu;


Ngati tilandira umboni wa anthu, umboni wa Mulungu uposa; chifukwa umboni wa Mulungu ndi uwu, kuti anachita umboni za Mwana wake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa