1 Yohane 3:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo mudziwa kuti Iyeyu anaonekera kudzachotsa machimo; ndipo mwa Iye mulibe tchimo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo mudziwa kuti Iyeyu anaonekera kudzachotsa machimo; ndipo mwa Iye mulibe tchimo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Mukudziŵa kuti Khristu adaoneka kuti adzachotse machimo, ndipo mwa Iye mulibe tchimo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Koma inu mukudziwa kuti Yesu anabwera kuti adzachotse machimo athu. Ndipo mwa Iye mulibe tchimo. Onani mutuwo |