1 Yohane 3:4 - Buku Lopatulika4 Yense wakuchita tchimo achitanso kusaweruzika; ndipo tchimo ndilo kusaweruzika. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Yense wakuchita tchimo achitanso kusaweruzika; ndipo tchimo ndilo kusaweruzika. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Aliyense amene amachimwa, alinso ndi mlandu wa kuphwanya malamulo. Paja kuchimwa nkuphwanya malamulo kumene. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Aliyense amene amachimwa amaphwanya lamulo; pakuti tchimo ndi kuphwanya lamulo. Onani mutuwo |