1 Yohane 3:6 - Buku Lopatulika6 Yense wakukhala mwa Iye sachimwa; yense wakuchimwa sanamuone Iye, ndipo sanamdziwe Iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Yense wakukhala mwa Iye sachimwa; yense wakuchimwa sanamuona Iye, ndipo sanamdziwa Iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Munthu aliyense wokhala mwa Khristu, sachimwa. Aliyense amene amachimwa, sadamuwone ndipo sadamdziŵe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Aliyense wokhala mwa Khristu sachimwa. Aliyense amene amachimwa sanamuone kapena kumudziwa. Onani mutuwo |