1 Timoteyo 3:3 - Buku Lopatulika3 wosati woledzera, kapena womenyana ndeu; komatu wofatsa, wopanda ndeu, wosakhumba chuma; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 wosati woledzera, kapena womenyana ndeu; komatu wofatsa, wopanda ndeu, wosakhumba chuma; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Asakhale chidakwa, asakhale wandeu, koma wofatsa, wosakangana ndi anthu, ndi wosakonda ndalama. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Asakhale chidakwa, asakhale wandewu, koma wofatsa, asakhale wokonda mikangano, kapena wokonda ndalama. Onani mutuwo |