1 Samueli 9:2 - Buku Lopatulika2 Iye anali ndi mwana wamwamuna dzina lake Saulo, mnyamata wokongola; pakati pa anthu onse a Israele panalibe wina wokongola ngati iye; anali wamtali, anthu ena onse anamlekeza m'chifuwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Iye anali ndi mwana wamwamuna dzina lake Saulo, mnyamata wokongola; pakati pa anthu onse a Israele panalibe wina wokongola ngati iye; anali wamtali, anthu onse ena anamlekeza m'chifuwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Iyeyo anali ndi mwana dzina lake Saulo, mnyamata wokongola. Pakati pa Aisraele onse panalibenso mnyamata wokongola kupambana iyeyo. Anali wamtali kotero kuti anthu ena onse ankamugwa m'mapewa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Iyeyu anali ndi mwana dzina lake Sauli, mnyamata wa maonekedwe abwino. Pakati pa Aisraeli onse panalibe wofanana naye. Anali wamtali kotero kuti anthu onse ankamulekeza mʼmapewa. Onani mutuwo |