Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 9:18 - Buku Lopatulika

18 Pomwepo Saulo anayandikira kwa Samuele pakati pa chipata, nati, Mundidziwitse nyumba ya mlauliyo ili kuti.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Pomwepo Saulo anayandikira kwa Samuele pakati pa chipata, nati, Mundidziwitse nyumba ya mlauliyo ili kuti.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Tsono Saulo adayandikira Samueleyo ku chipata namufunsa kuti, “Zikomo, kodi kunyumba kwa mlosi nkuti?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Tsono Sauli anayandikira Samueli pa chipata ndipo anamufunsa, “Kodi mungandiwuze kumene kuli nyumba ya mlosi?”

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 9:18
2 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene Samuele anaona Saulo, Yehova anati kwa iye, Ona munthu amene ndinakuuza za iye! Ameneyu adzaweruza anthu anga.


Ndipo Samuele anayankha Saulo nati, Ine ndine mlauliyo. Kwera, batsogola kumsanje, pakuti mudzadya ndi ine lero; ndipo m'mawa ndidzakulola upite, ndi kukudziwitsa zonse zili mumtima mwako.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa