1 Samueli 9:17 - Buku Lopatulika17 Ndipo pamene Samuele anaona Saulo, Yehova anati kwa iye, Ona munthu amene ndinakuuza za iye! Ameneyu adzaweruza anthu anga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Ndipo pamene Samuele anaona Saulo, Yehova anati kwa iye, Ona munthu amene ndinakuuza za iye! Ameneyu adzaweruza anthu anga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Samuele ataona Saulo, Chauta adamuuza kuti, “Ndi ameneyu munthu ndidakuuza uja. Ndiye amene adzalamulire anthu anga.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Samueli atamuona Sauli, Yehova anamuwuza kuti, “Munthu ndinakuwuza uja ndi uyu. Iyeyu adzalamulira anthu anga.” Onani mutuwo |