Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 9:14 - Buku Lopatulika

14 Ndipo iwowa anakwera kumzinda; ndipo m'mene analowa m'mzindamo, onani, Samuele anatulukira pali iwo, kuti akakwere kumsanje.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

14 Ndipo iwowa anakwera kumudzi; ndipo m'mene analowa m'mudzimo, onani, Samuele anatulukira pali iwo, kuti akakwere kumsanje.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

14 Choncho adapita kumzindako. Poloŵa mumzindamo, adaona Samuele akutuluka kumene, alikudza kwa iwo pa njira yopita kukachisi kuja.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

14 Choncho anapita ku mzinda kuja. Akulowa mu mzindamo, anaona Samueli akutuluka mu mzindamo akubwera kumene kunali iwo, koma amapita ku phiri, ku malo wopatulika.

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 9:14
2 Mawu Ofanana  

mutafika m'mzinda, pomwepo mudzampeza, asanakwere kumsanje kukadya; pakuti anthu sadzadya, koma iye atafika ndipo; pakuti iye amadalitsa nsembeyo; ndipo atatero oitanidwawo amadya. Chifukwa chake kwerani; popeza nthawi ino mudzampeza.


Ndipo Yehova anaululiratu m'khutu la Samuele dzulo lake la tsiku limene Saulo anabwera, kuti,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa